Lyrics

[Lyrics] Wikise – Belu

INTRO

Owuooooh

Owuooooooooooh

Owuowoooooo (Emama namalenga eeh)

Owuooooh

Owuooooooooooh

Owuowoooooo (ambuye namalenga baba)

VERSE 1

Satana walisochelesa dziko (kuno)

Zinthu zoipa anthu ayesa zabwino (nyasi)

Koma ambuye zili kuno

Anthu akonda ndalama

Kuposa moyo wa munthu

Akakhuta migayiwa

Mayambisa timabungwe ati orphanage chani chani

Akalandila fund

Kumagula tima mira

Nkumati shanila (nkumatilanda akazi)

Can you imagine ambuye

Azimayi oyima kuseli kwa crossroads

mpaka kukhala ndi association

Kumapanga mademo

Enough is enough basi

CHORUS

Ambuye Imbani Belu uu

Description: 🔔

Nthawiiiiii

Dziko kuno laonongeka aaah (dziko lanunkha enough is enough basi?

Yehova Imbani Belu uuDescription: 🔔

Nthawi iii

Dziko kuno laonongeka aaah (dziko lanunkha)

VERSE 2

Atumiki anu anakutulukani

Amangolalikira za ndalama

Dzina lanu pano ndi mpamba

Imbani lipengalo lilire

(Trumpet)

Akumatiuza pelekani molowa manja

Ulemelero wathu uli Kumwamba

Iwo namagula magalimoto

Ife namayenda napatapata

Musatemero Angelo

Ingoyimbani belu

Anthu chilungamo pansi

Angelo anu azawadyesa Banzi.

BACK TO CHORUS

Ambuye Imbani Belu uuDescription: 🔔

Nthawiiiiii

Dziko kuno laonongeka aaah (dziko lanunkha enough is enough basi?

Yehova Imbani Belu uuDescription: 🔔

Nthawi iii

Dziko kuno laonongeka aaah (dziko lanunkha)

OUTRO

Achuluka ndi adyela

Opondeleza Imbani belu baba

THE END

MRB Reporter

Do you want your song or Article to be featured on this Publication or do you want to advertise with us? For inquiries contact malawianrapbattle@gmail.com

Related Articles

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *