Lyrics

Toria – Birimankhwe Lyrics

[Intro];
Yeah, people these days change like Chameleons you know. They change, depending on where they are…. (((((Toriah)))))

(Verse 1);
Ndinafera mawanga ankhanga/ Ndinkati ndapeza mzanga/ Kumuwonetsa kwa amzanga/ Osadziwa ndikudziyika ndekha pa Minga eeeeh/
Yeah i know Nobody is perfect// Nane ndiri ndi zofowoka//
Ndife anthu, sife nyama, ndichifukwa chake tinkakhala kukambirana//

Mtima wamzako ndi tsidya lina aaah// Ukamupepesa ati Nkhani yatha aaah// Osadziwa akusunguira adha, Nkhonya yobwezera imawawa sananame aja//

(Hook);
Munthu ndi Birimankhwe/ Munthudi amasintha aaaaah///
Munthu ndi Birimankhwe, amasintha kutengera ndipomwe wafikapo// X2….

(Verse 2);
Sindinakwatire ndi chi Messi ine/ Sindinakwatire ndi chi Ronaldo/ Zomandiyenda Njomba ine ayi, ndatopa kukhalira kumwa Panado//
Ndatiii, Sindinakwatire ndi chi Under taker, sindinakwatire ndi chi John Cena//
Ngati watopa nane peza wina/ Mwina nanenso ndingawone zina//

Banja ndinalifuna, koma bambowa kumenya//
Dziko lake lomweri, koma ngati ndiri ku Kenya//
Asawone chinthu, pompopompo kundikwenya//
Sonu Nthena, nilolani niyendepo apa//

((((((((Back to chorus))))))))

(Verse 3)
Ndikanakonda nkanakhala ine, nanu mpaka kale//
Koma Zawonjeza, ndichani ndinalakwa ineee//
Tachokadi kutali bambo a Juh, koma tisiyane// Ndikanakonda ndikanakhala, ndikanakhala, nanu Mpaka kale//////

((((((Back to Chorus(hook))))))))))))))))))))))))))))))))))))

MRB Reporter

Do you want your song or Article to be featured on this Publication or do you want to advertise with us? For inquiries contact malawianrapbattle@gmail.com

Related Articles

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *