International News

Dziko la Sudan lipanga Ubale Ndi Zigawenga zama Gulu Asanu

Dziko la Sudan lero lasainirana pangano la mtendere ndi gulu lazigawenga lochokera ku Darful.

Mwambowo udachitikira mdziko la South Sudan ndipo mkhara pakati adari Mtsogoleri wadziko la South Sudan Salva Kiir. Komanso Prime Minister wa Sudan Abdallah Hamdok ndi akuluakulu ena.

Mdziko la Sudan mwakhara mulinkhondo yapachiweniweni kwazaka khumi.

Anthu ambiri adafa komanso kuthawa mdzikolo zaka zambuyomu.

MRB Reporter

Do you want your song or Article to be featured on this Publication or do you want to advertise with us? For inquiries contact malawianrapbattle@gmail.com

Related Articles

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *