Lyrics

Zimveke Bwa? Lyrics

Zimveke Bwa? Lyrics

uuh muti zimveke bwa? uh huh

H-Y-P-H…

Hyphen verse 1

ah ah ukukaika

chiphona chogona, chi master chomaliza

huh, chi mfana cholaiva, chosaimva

olo Ichocho ku saizaaa

osaphweketsa we rarely socialize

positive vibes we polarize

musunge chithumba if ever you call on us

bruh every building we been in we colonize

bar after bar after bar chiku charger

kuthuzula, kuphuzula ngati Mchacha

look who you are, never been part of the culture

mafana okula mosemphana ndi makhatcha

chorus

Inu mmati zimveke bwa?

mwaputa olakwika mupweteka

osamangotamika kuphweketsa

sitiyimva, lero mupepesa, mupepesa

Hyphen verse 2

nde, nde nkachekela, tchekela

khonfi yangolomela kutelela

kamunthu umakakondako, tsekela

kujama ya ife uzaona polekela

take shots popanda kuphelela

take notes mafana akuchepela

zikawawa tisanza, sitimezela

tikakunyala tiku halla sitizembelaaa

mafana a tchubu otilemela

play the part sitidanda zotisemela

ka utsi kazomelela, ka mwano kutiyenela

nthano zanuzo mukuti zimveke bwa?

Achina Gattah Verse 3

yoh, show ya usiku ndi ma G

koma zomwe zachitika iwe iiih

kuchezela kuyatsa moto ngati ovuni

ine ndi smoke aise ndi fake mchumuni

ndinasowa pakati ndinavaya,

ndimakagwila bele kwa yaya

mwina sumadziwa ndinazama man

nkona ndiku hitta kuposa nyimbo za ma man

koma, mafana adhiwawa, kupandipanga nkhanza man

dzulo ndakumana ndi Mandela pa Mwanza man

akuti a Gattah muli sick mukusanza man

ndati eeh ndimatha kwambiri ndine sanza man

ngati Ice Prince, udolo nnamaliza man

streets is safe I run

iwe, ndani akupanga makani

Inu, ckuf you all I’m done

MRB Reporter

Do you want your song or Article to be featured on this Publication or do you want to advertise with us? For inquiries contact malawianrapbattle@gmail.com

Related Articles